Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 2:18 - Buku Lopatulika

Ndipo anthu onse amene anamva anazizwa ndi zinthu abusa adalankhula nao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anthu onse amene anamva anazizwa ndi zinthu abusa adalankhula nao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Onse amene ankamva, ankadabwa ndi zimene abusawo ankaŵasimbira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo onse amene anamva zimene abusawa ananena anadabwa.

Onani mutuwo



Luka 2:18
8 Mawu Ofanana  

Taonani, ine ndi ana amene Yehova wandipatsa ine, tili zizindikiro ndi zodabwitsa mwa Israele, kuchokera kwa Yehova wa makamu, amene akhala m'phiri la Ziyoni.


Ndipo iwo, m'mene anaona, anadziwitsa anthu za mau analankhulidwa kwa iwo a mwana uyu.


Koma Maria anasunga mau awa onse, nawalingalira mumtima mwake.


Ndipo atate ndi amake anali kuzizwa ndi zinthu zolankhulidwa za Iye.


Ndipo onse amene anamva Iye anadabwa ndi chidziwitso chake, ndi mayankho ake.


Ndipo anthu onse anadabwa, nalankhulana wina ndi mnzake, nanena, Mau amenewa ali otani? Chifukwa ndi ulamuliro ndi mphamvu angolamulira mizimu yonyansa, ndipo ingotuluka.