Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 19:16 - Buku Lopatulika

Ndipo anafika woyamba, nanena, Mbuye, mina yanu inachita nionjeza mina khumi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anafika woyamba, nanena, Mbuye, mina yanu inachita nionjeza mina khumi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Woyamba adadza nati, ‘Ambuye, ndalama yanu ija idapindula ndalama makumi khumi.’

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Woyamba anabwera ndipo anati, ‘Bwana ndalama zanu zapindula khumi zina.’

Onani mutuwo



Luka 19:16
8 Mawu Ofanana  

Ndipo anaitana akapolo ake khumi, nawapatsa iwo ndalama khumi za mina, nati kwaiwo, Chita nazoni malonda kufikira ndibweranso.


Ndipo kunali, pakubwera iye, atalandira ufumuwo, anati aitanidwe kwa iye akapolo aja, amene adawapatsa ndalamazo, kuti adziwe umo anapindulira pochita malonda.


Ndipo anati kwa iye, Chabwino, kapolo wabwino iwe; popeza unakhala wokhulupirika m'chaching'onong'ono, khala nao ulamuliro pa mizinda khumi.


Koma ndi chisomo cha Mulungu ndili ine amene ndili; ndipo chisomo chake cha kwa ine sichinakhale chopanda pake, koma ndinagwirira ntchito yochuluka ya iwo onse; koma si ine, koma chisomo cha Mulungu chakukhala ndi ine.