Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 18:6 - Buku Lopatulika

Ndipo Ambuye anati, Tamverani chonena woweruza wosalungama.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Ambuye anati, Tamverani chonena woweruza wosalungama.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Ambuye adati, “Mwamvatu mau a woweruza wosalungama uja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Ambuye anati, “Tamvani zimene woweruza wopanda chilungamoyu wanena.

Onani mutuwo



Luka 18:6
4 Mawu Ofanana  

kotero kuti mukakhale ana a Atate wanu wa Kumwamba; chifukwa Iye amakwezera dzuwa lake pa oipa ndi pa abwino, namavumbitsira mvula pa olungama ndi pa osalungama.


Ndipo pamene Ambuye anamuona, anagwidwa ndi chifundo chifukwa cha iye, nanena naye, Usalire.


Ndipo Yohane anaitana awiri a ophunzira ake, nawatuma kwa Ambuye, nanena, Kodi ndinu wakudzayo, kapena tiyang'anire wina?


kodi simunasiyanitse mwa inu nokha, ndi kukhala oweruza oganizira zoipa?