Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 18:41 - Buku Lopatulika

Ufuna ndikuchitire chiyani? Ndipo anati, Ambuye, kuti ndipenyenso.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ufuna ndikuchitire chiyani? Ndipo anati, Ambuye, kuti ndipenyenso.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Kodi ukufuna kuti ndikuchitire chiyani?” Iye adati, “Ambuye, ndikufuna kuti ndizipenyanso.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Kodi ukufuna kuti ndikuchitire chiyani?” Iye anayankha kuti, “Ambuye, ine ndifuna ndionenso.”

Onani mutuwo



Luka 18:41
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anaima, nalamulira kuti abwere naye kwa Iye; ndipo m'mene adafika pafupi, anamfunsa iye,


Ndipo Yesu anati kwa iye, Penyanso: chikhulupiriro chako chakupulumutsa iwe.


Koma ngati tiyembekezera chimene sitichipenya, pomwepo tichilindirira ndi chipiriro.


Musadere nkhawa konse; komatu m'zonse ndi pemphero, ndi pembedzero, pamodzi ndi chiyamiko, zopempha zanu zidziwike kwa Mulungu.