Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 18:34 - Buku Lopatulika

Ndipo sanadziwitse kanthu ka izi; ndi mau awa adawabisikira, ndipo sanazindikire zonenedwazo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo sanadziwitse kanthu ka izi; ndi mau awa adawabisikira, ndipo sanazindikire zonenedwazo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ophunzira aja sadamvetse konse zimenezi. Tanthauzo la mau ameneŵa linali lobisika kwa iwo, nchifukwa chake sadamvetsetse zimene Yesu ankanenazo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ophunzira sanazindikire china chilichonse cha izi. Tanthauzo lake linabisika kwa iwo, ndipo sanadziwe chimene Iye amayankhula.

Onani mutuwo



Luka 18:34
9 Mawu Ofanana  

Koma iwo sanazindikire mauwo, naopa kumfunsa.


ndipo atamkwapula adzamupha Iye; ndipo tsiku lachitatu adzauka.


Ndipo sanadziwitse mau amene Iye analankhula nao.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Opusa inu, ndi ozengereza mtima kusakhulupirira zonse adazilankhula aneneri!


Ndipo anawatsegulira mitima yao, kuti adziwitse malembo;


Koma iwo sanadziwitse mau awa, ndipo anabisidwa kwa iwo, kuti asawadziwe; ndipo anaopa kumfunsa za mau awa.


Fanizo ili Yesu ananena kwa iwo; koma sanazindikire zimene Yesu analikulankhula nao.


Izi sanazidziwe ophunzira ake poyamba; koma pamene Yesu analemekezedwa, pamenepo anakumbukira kuti izi zinalembedwa za Iye, ndi kuti adamchitira Iye izi.