Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 18:2 - Buku Lopatulika

nanena, M'mzinda mwakuti munali woweruza wosaopa Mulungu, ndi wosasamala munthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

nanena, M'mudzi mwakuti munali woweruza wosaopa Mulungu, ndi wosasamala munthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adati, “M'mudzi mwina mudaali woweruza wina amene sankaopa Mulungu kapena kulabadako za munthu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anati, “Mʼmudzi wina munali woweruza wosaopa Mulungu ngakhalenso kulabadira za anthu.

Onani mutuwo



Luka 18:2
14 Mawu Ofanana  

Wolungama asamalira mlandu wa osauka; koma woipa alibe nzeru yakuudziwa.


Njira zamakwalala zikufa, kulibe woyendamo; Asiriya wathyola chipangano, wanyoza mizinda, sasamalira anthu.


Ndipo m'mzinda momwemo munali mkazi wamasiye; ndipo anadza kwa iye nanena, Mundiweruzire mlandu pa wotsutsana nane.


Ndipo sanafune nthawi; koma bwinobwino anati mwa yekha, Ndingakhale sindiopa Mulungu kapena kusamala munthu;


Ndipo mwini mundawo anati, Ndidzachita chiyani? Ndidzatuma mwana wanga amene ndikondana naye; kapena akamchitira iye ulemu.


Komanso, tinali nao atate a thupi lathu akutilanga, ndipo tinawalemekeza; kodi sitidzagonjera Atate wa mizimu koposa nanga, ndi kukhala ndi moyo?