Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 17:5 - Buku Lopatulika

Ndipo atumwi anati kwa Ambuye, Mutionjezere chikhulupiriro.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo atumwi anati kwa Ambuye, Mutionjezere chikhulupiriro.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Atumwi adapempha Ambuye kuti, “Mutiwonjezere chikhulupiriro.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atumwiwo anati kwa Ambuye, “Kulitsani chikhulupiriro chathu!”

Onani mutuwo



Luka 17:5
9 Mawu Ofanana  

Ndipo atumwi anasonkhana kwa Yesu; namuuza zilizonse adazichita, ndi zonse adaziphunzitsa.


Pomwepo atate wa mwana anafuula, nanena, Ndikhulupirira; thandizani kusakhulupirira kwanga.


Ndipo pamene Ambuye anamuona, anagwidwa ndi chifundo chifukwa cha iye, nanena naye, Usalire.


Ndipo Yohane anaitana awiri a ophunzira ake, nawatuma kwa Ambuye, nanena, Kodi ndinu wakudzayo, kapena tiyang'anire wina?


Ndikhoza zonse mwa Iye wondipatsa mphamvuyo.


Tiziyamika Mulungu nthawi zonse chifukwa cha inu, abale, monga kuyenera; pakuti chikhulupiriro chanu chikula chikulire, ndipo chichulukira chikondano cha inu nonse, yense pa mnzake;


Yesu, ameneyo, chifukwa cha chimwemwe choikidwacho pamaso pake, anapirira mtanda, nanyoza manyazi, nakhala padzanja lamanja la mpando wachifumu wa Mulungu.