Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 17:18 - Buku Lopatulika

Akubwera kulemekeza Mulungu sanapezeke mmodzi kodi, koma mlendo uyu?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Akubwera kulemekeza Mulungu sanapezeka mmodzi kodi, koma mlendo uyu?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndiye kuti sadabwerere wina aliyense kudzayamika Mulungu, koma mlendo yekhayu?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kodi palibe mmodzi mwa iwo amene anabwerera kudzalemekeza Mulungu kupatula mlendoyu?”

Onani mutuwo



Luka 17:18
12 Mawu Ofanana  

Koma anaiwala ntchito zake msanga; sanalindire uphungu wake:


Wopereka nsembe yachiyamiko andilemekeza Ine; ndipo kwa iye wosunga mayendedwe ake ndidzamuonetsa chipulumutso cha Mulungu.


Apereke ulemerero kwa Yehova, anene matamando ake m'zisumbu.


Koma ambiri oyamba adzakhala akuthungo, ndi akuthungo adzakhala oyamba.


Chomwecho omalizira adzakhala oyamba, ndipo oyamba adzakhala omalizira.


Ndipo pakumva ichi, Yesu anazizwa, nati kwa iwo akumtsata, Indetu ndinena kwa inu, ngakhale mwa Israele, sindinapeze chikhulupiriro chotere.


koma anawo a Ufumu adzatayidwa kumdima wakunja; komweko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.


Ndipo m'mene anthu a makamu anachiona, anaopa, nalemekeza Mulungu, wakupatsa anthu mphamvu yotere.


Ndipo Yesu anayankha nati, Kodi sanakonzedwe khumi? Koma ali kuti asanu ndi anai aja?


ndi kunena ndi mau aakulu, Opani Mulungu, mpatseni ulemerero; pakuti yafika nthawi ya chiweruziro chake; ndipo mlambireni Iye amene analenga kumwamba ndi dziko lapansi ndi nyanja ndi akasupe amadzi.