Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 17:13 - Buku Lopatulika

ndipo iwo anakweza mau, nanena, Yesu, Mbuye, mutichitire chifundo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo iwo anakweza mau, nanena, Yesu, Mbuye, mutichitire chifundo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

nanena mokweza mau kuti, “Yesu Ambuye, tichitireni chifundo.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo anafuwula ndi mawu okweza kuti, “Yesu, Ambuye, tichitireni chifundo!”

Onani mutuwo



Luka 17:13
7 Mawu Ofanana  

Ndipo onani, mkazi wa ku Kanani anatuluka m'malire, nafuula, nati, Mundichitire ine chifundo Ambuye, mwana wa Davide; mwana wanga wamkazi wagwidwa koopsa ndi chiwanda.


Ndipo popita Yesu kuchokera kumeneko, anamtsata Iye anthu awiri akhungu, ofuula ndi kuti, Mutichitire ife chifundo, mwana wa Davide.


Ndipo kawirikawiri ukamtaya kumoto ndi kumadzi, kumuononga; koma ngati mukhoza kuchita kanthu mtithandize, ndi kutichitira chifundo.


Ndipo pakuwaona anati kwa iwo, Pitani, kadzionetseni nokha kwa ansembe. Ndipo kunali, m'kumuka kwao, anakonzedwa.


Ndipo Simoni anayankha, nati, Ambuye, tinagwiritsa ntchito usiku wonse osakola kanthu, koma pa mau anu ndidzaponya makoka.