Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 15:1 - Buku Lopatulika

Koma amisonkho onse ndi anthu ochimwa analikumyandikira kudzamva Iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma amisonkho onse ndi anthu ochimwa analikumyandikira kudzamva Iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu onse okhometsa msonkho ndi Ayuda enanso onyozera Malamulo ankabwera kwa Yesu kudzamva mau ake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsopano amisonkho ndi “ochimwa” ankasonkhana kudzamvera mawu ake.

Onani mutuwo



Luka 15:1
9 Mawu Ofanana  

Ndipo woipayo akatembenukira kuleka choipa chake adachichita, nakachita chiweruzo ndi chilungamo, adzapulumutsa moyo wake.


Chifukwa kuti ngati muwakonda akukondana ndi inu mphotho yanji muli nayo? Kodi angakhale amisonkho sachita chomwecho?


Ndipo onani, alipo akuthungo amene adzakhala oyamba, ndipo alipo oyamba adzakhala akuthungo.


Ndipo anthu onse ndi amisonkho omwe, pakumva, anavomereza kuti Mulungu ali wolungama, popeza anabatizidwa iwo ndi ubatizo wa Yohane.


Ndipo lamulo linalowa moonjezera, kuti kulakwa kukachuluke; koma pamene uchimo unachuluka, pomwepo chisomo chinachuluka koposa;


Mauwa ali okhulupirika ndi oyenera konse kuti awalandire, kuti Khristu Yesu anadza kudziko lapansi kupulumutsa ochimwa; wa iwowa ine ndine woposa;