Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 14:6 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo sanathe kumbwezera mau pa zinthu izi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo sanathe kumbwezera mau pa zinthu izi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iwo adasoŵa poyankha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo iwo analibe choyankha.

Onani mutuwo



Luka 14:6
6 Mawu Ofanana  

Ndipo sanalimbike mtima munthu aliyense kumfunsa kanthu kuyambira tsiku lomwelo.


Ndipo pamene Iye anatero, onse aja akutsutsana naye ananyazitsidwa; ndipo anthu onse a m'khamu anakondwera ndi zinthu zonse za ulemererozo zinachitidwa ndi Iye.


Ndipo sanakhoze kugwira mauwo pamaso pa anthu; ndipo anazizwa ndi kuyankha kwake, nakhala chete.


Pakuti sanalimbenso mtima kumfunsa Iye kanthu kena.


Pakuti Ine ndidzakupatsani inu kamwa ndi nzeru, zimene adani anu onse sadzatha kuzikana kapena kuzitsutsa.


Ndipo sanathe kuipambana nzeru ndi Mzimu amene analankhula naye.