Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 14:4 - Buku Lopatulika

Koma iwo anakhala chete. Ndipo anamtenga namchiritsa, namuuza apite.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma iwo anakhala chete. Ndipo anamtenga namchiritsa, namuuza apite.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma iwo adangoti chete. Tsono Yesu adatenga munthuyo, ndipo atamchiritsa, adamuuza kuti azipita.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma iwo sanayankhe. Tsono atamutenga munthuyo, Iye anamuchiritsa ndipo anamuwuza kuti azipita.

Onani mutuwo



Luka 14:4
4 Mawu Ofanana  

Ndipo sanalimbike mtima munthu aliyense kumfunsa kanthu kuyambira tsiku lomwelo.


Ndipo Yesu anayankha nati kwa achilamulo ndi Afarisi, nanena, Kodi nkuloledwa tsiku la Sabata kuchiritsa, kapena iai?


Ndipo anati kwa iwo, Ndani wa inu bulu wake kapena ng'ombe yake itagwa m'chitsime, ndipo sadzaitulutsa pomwepo tsiku la Sabata kodi?