Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 13:30 - Buku Lopatulika

Ndipo onani, alipo akuthungo amene adzakhala oyamba, ndipo alipo oyamba adzakhala akuthungo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo onani, alipo akuthungo amene adzakhala oyamba, ndipo alipo oyamba adzakhala akuthungo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo amene ali otsirizira adzakhala oyambirira, ndipo amene ali oyambirira adzakhala otsirizira.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndithudi otsirizira ndiye adzakhale oyambirira, ndipo oyambirira ndiye adzakhale otsirizira.”

Onani mutuwo



Luka 13:30
6 Mawu Ofanana  

Koma ambiri oyamba adzakhala akuthungo, ndi akuthungo adzakhala oyamba.


Chomwecho omalizira adzakhala oyamba, ndipo oyamba adzakhala omalizira.


Koma ambiri akuyamba adzakhala akuthungo, ndi akuthungo adzakhala oyamba.