Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 13:20 - Buku Lopatulika

Ndiponso anati, Ndidzafanizira Ufumu wa Mulungu ndi chiyani?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndiponso anati, Ndidzafanizira Ufumu wa Mulungu ndi chiyani?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adatinso, “Ndingayerekezenso ndi chiyani Ufumu wa Mulungu?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anafunsanso kuti, “Kodi ufumu wa Mulungu ndingawufanizire ndi chiyani?

Onani mutuwo



Luka 13:20
4 Mawu Ofanana  

Koma ndidzafanizira ndi chiyani obadwa awa a makono? Ali ofanana ndi ana akukhala m'mabwalo a malonda, amene alikuitana anzao.


Fanizo lina Iye anawafotokozera iwo, nanena, Ufumu wa Kumwamba ufanizidwa ndi munthu, amene anafesa mbeu zabwino m'munda mwake;


Pamenepo ananena, Ufumu wa Mulungu ufanana ndi chiyani? Ndipo ndidzaufanizira ndi chiyani?


Ufanana ndi chotupitsa mikate, chimene mkazi anatenga, nachibisa mu miyeso itatu ya ufa, kufikira unatupo wonsewo.