Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 13:10 - Buku Lopatulika

Ndipo analikuphunzitsa m'sunagoge mwina, tsiku la Sabata.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo analikuphunzitsa m'sunagoge mwina, tsiku la Sabata.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsiku lina la Sabata Yesu ankaphunzitsa m'nyumba ina yamapemphero.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa Sabata Yesu ankaphunzitsa mʼsunagoge ina,

Onani mutuwo



Luka 13:10
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anayendayenda mu Galileya monse, analikuphunzitsa m'masunagoge mwao, nalalikira Uthenga Wabwino wa Ufumu, nachiritsa nthenda zonse ndi kudwala konse mwa anthu.


ndipo ngati udzabala chipatso kuyambira pamenepo, chabwino; koma ngati iai, mudzaulikhatu.


Ndipo Iye analikulalikira m'masunagoge a ku Yudeya.