Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 12:57 - Buku Lopatulika

Ndipo inunso, pa nokha mulekeranji kuweruza kolungama?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo inunso, pa nokha mulekeranji kuweruza kolungama?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Bwanji simutsimikiza nokha zoyenera kuchita?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Bwanji simukuzindikira nokha zoyenera kuchita?

Onani mutuwo



Luka 12:57
10 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iwo, Indedi ndinena kwa inu, Ngati mukhala nacho chikhulupiriro, osakayikakayika, mudzachita si ichi cha pa mkuyu chokha, koma ngati mudzati ngakhale kuphiri ili, Tanyamulidwa, nuponyedwe m'nyanja, chidzachitidwa.


Popeza Yohane anadza kwa inu m'njira ya chilungamo, ndipo simunamvere iye; koma amisonkho ndi akazi achiwerewere anammvera iye; ndipo inu, m'mene munachiona, simunalape pambuyo pake, kuti mumvere iye.


pamene iphukira, muipenya nimuzindikira pa nokha kuti dzinja lili pafupi pomwepo.


Musaweruze monga maonekedwe, koma weruzani chiweruziro cholungama.


Ndipo ndi mau ena ambiri anachita umboni, nawadandaulira iwo, nanena, Mudzipulumutse kwa mbadwo uno wokhotakhota.


Lingirirani mwa inu nokha: Kodi nkuyenera kuti apemphere kwa Mulungu, wosafunda mutu?


Kodi ubadwidwe womwe sutiphunzitsa kuti ngati mwamuna aweta tsitsi chinyozetsa iye?


Akadakhala nazo nzeru, akadazindikira ichi, akadasamalira chitsirizo chao!