Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 12:44 - Buku Lopatulika

Ndinena ndinu zoona, kuti adzamuika iye kapitao wa pa zonse ali nazo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndinena ndinu zoona, kuti adzamuika iye kapitao wa pa zonse ali nazo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndithu ndikunenetsa kuti adzamuika woyang'anira chuma chake chonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti adzamuyika kukhala woyangʼanira katundu wake yense.

Onani mutuwo



Luka 12:44
8 Mawu Ofanana  

Indetu, ndinena kwa inu, kuti adzamkhazika iye woyang'anira zinthu zake zonse.


Mbuye wake anati kwa iye, Chabwino, kapolo iwe wabwino ndi wokhulupirika; unali wokhulupirika pa zinthu zazing'ono, ndidzakhazika iwe pa zinthu zambiri; lowa iwe m'chikondwerero cha mbuye wako.


Wodala kapoloyo amene mbuye wake pakufika, adzampeza alikuchita chotero.


Koma kapolo uyo akanena mumtima mwake, Mbuye wanga azengereza kudza; ndimo akayamba kupanda anyamata ndi adzakazi ndi kudya ndi kumwa, ndi kuledzera;


ndikulangiza ugule kwa Ine golide woyengeka m'moto, kuti ukakhale wachuma, ndi zovala zoyera, kuti ukadziveke, ndi kuti manyazi a usiwa wako asaoneke; ndi mankhwala opaka m'maso mwako, kuti ukaone.