Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 12:34 - Buku Lopatulika

Pakuti kumene kuli chuma chanu, komweko kudzakhalanso mtima wanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti kumene kuli chuma chanu, komweko kudzakhalanso mtima wanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pajatu kumene kuli chuma chako, mtima wakonso kokhala nkomweko.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Popeza kumene kuli chuma chanu, mtima wanunso udzakhala komweko.”

Onani mutuwo



Luka 12:34
4 Mawu Ofanana  

pakuti kumene kuli chuma chako, komwe udzakhala mtima wakonso.


Khalani odzimangira m'chuuno, ndipo nyali zanu zikhale zoyaka;


Pakuti ufulu wathu uli Kumwamba; kuchokera komwenso tilindirira Mpulumutsi, Ambuye Yesu Khristu;