Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 11:6 - Buku Lopatulika

popeza wandidzera bwenzi langa lochokera paulendo ndipo ndilibe chompatsa;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

popeza wandidzera ndipo ndilibe chompatsa;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kwafika bwenzi langa, ali pa ulendo, ndipo ndilibe choti ndingampatse.’

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

chifukwa ndalandira bwenzi langa amene ali pa ulendo ndipo ine ndilibe choti ndimupatse.’

Onani mutuwo



Luka 11:6
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anati kwa iwo, Ndani wa inu adzakhala ndi bwenzi lake, nadzapita kwa iye pakati pa usiku, nadzati kwa iye, Bwenzi, ndibwereke mikate itatu;


ndipo iyeyu wa m'katimo poyankha akati, Usandivuta; pakhomo mpotseka tsopano, ndipo ana anga ali nane pamodzi pogona; sindingathe kuuka ndi kukupatsa?