Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 11:47 - Buku Lopatulika

Tsoka inu! Chifukwa mumanga za pa manda a aneneri, ndipo makolo anu anawapha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tsoka inu! Chifukwa mumanga za pa manda a aneneri, ndipo makolo anu anawapha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Muli ndi tsoka, chifukwa mumamanga ziliza za aneneri, pamene ndi makolo anu omwe akale amene adapha aneneriwo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Tsoka kwa inu, chifukwa mumawaka manda a aneneri, komatu ndi makolo anu amene anawapha.

Onani mutuwo



Luka 11:47
5 Mawu Ofanana  

Tsoka inu, alembi ndi Afarisi, onyenga! Chifukwa mufanafana ndi manda opaka njereza, amene aonekera okoma kunja kwake, koma adzala m'katimo ndi mafupa a anthu akufa ndi zonyansa zonse.


Chomwecho muli mboni, ndipo muvomera ntchito za makolo anu; chifukwa iwotu anawapha, koma inu muwamangira iwo zapamanda.


Ouma khosi ndi osadulidwa mtima ndi makutu inu, mukaniza Mzimu Woyera nthawi zonse; monga anachita makolo anu, momwemo inu.


amene adaphanso Ambuye Yesu, ndi aneneri, natilondalonda ife, ndipo sakondweretsa Mulungu, natsutsana nao anthu onse;