Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 11:30 - Buku Lopatulika

Pakuti monga ngati Yona anali chizindikiro kwa Aninive, chotero adzakhalanso Mwana wa Munthu kwa mbadwo uno.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti monga ngati Yona anali chizindikiro kwa Aninive, chotero adzakhalanso Mwana wa Munthu kwa mbadwo uno.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Monga Yona uja anali chizindikiro kwa anthu a ku Ninive, chomwechonso Mwana wa Munthu adzakhala chizindikiro kwa anthu a mbadwo uno.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Monga Yona uja anali chizindikiro kwa anthu ku Ninive, momwemonso Mwana wa Munthu adzakhala chizindikiro kwa anthu a mʼbado uno.

Onani mutuwo



Luka 11:30
7 Mawu Ofanana  

Momwemo Ezekiele adzakhala kwa inu chizindikiro; umo monse anachitira iye mudzachita ndinu; chikadza ichi mudzadziwa kuti Ine ndine Ambuye Yehova.


Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yona mwana wa Amitai, ndi kuti,


Koma Yehova anaikiratu chinsomba chachikulu chimeze Yona; ndipo Yona anali m'mimba mwa nsombayi masiku atatu usana ndi usiku.


Pamenepo Yehova analankhula ndi nsombayo, ndipo inamsanzira Yona kumtunda.