Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 11:25 - Buku Lopatulika

ndipo pofika, uipeza yosesa ndi yokonzeka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo pofika, uipeza yosesa ndi yokonzeka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono ukafika, umapeza m'nyumba muja muli mosesasesa ndi mokonza bwino.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ukafika umapeza mʼnyumba mosesedwa bwino ndi mokonza.

Onani mutuwo



Luka 11:25
10 Mawu Ofanana  

Koma iwo akupatula kutsata njira zao zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi ochita zopanda pake. Mtendere ukhale pa Israele.


Mau a pakamwa pake ndiwo opanda pake ndi onyenga, waleka kuzindikira ndi kuchita bwino.


Pamene paliponse mzimu wonyansa ukatuluka mwa munthu, upyola malo opanda madzi nufunafuna mpumulo; ndipo posaupeza unena, Ndidzabwera kunyumba kwanga kumene ndinatulukako;


Pomwepo upita nutenga mizimu ina isanu ndi iwiri yoipa yoposa ndi uwu mwini; ndipo ilowa nikhalira komweko; ndipo makhalidwe otsiriza a munthu uyu aipa koposa oyambawo.