Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 11:16 - Buku Lopatulika

Koma ena anamuyesa, nafuna kwa Iye chizindikiro chochokera Kumwamba.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ena anamuyesa, nafuna kwa Iye chizindikiro chochokera Kumwamba.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Enanso pofuna kumuyesa, adampempha kuti aŵaonetse chizindikiro chozizwitsa chochokera kumwamba.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ena anamuyesa pomufunsa chizindikiro chochokera kumwamba.

Onani mutuwo



Luka 11:16
7 Mawu Ofanana  

Ndipo pakusonkhana pamodzi makamu a anthu, anayamba kunena, Mbadwo uno ndi mbadwo woipa; ufuna chizindikiro, ndipo chizindikiro sichidzapatsidwa kwa uwu koma chizindikiro cha Yona.


Chifukwa chake anati kwa Iye, Ndipo muchita chizindikiro chanji, kuti tione ndi kukhulupirira Inu? Muchita chiyani?


Koma ichi ananena kuti amuyese Iye, kuti akhale nacho chomneneza Iye. Koma Yesu, m'mene adawerama pansi analemba pansi ndi chala chake.


Ndipo popeza Ayuda afunsa zizindikiro, ndi Agriki atsata nzeru: