Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 11:11 - Buku Lopatulika

Ndipo ndani wa inu ali atate, mwana wake akadzampempha mkate, adzampatsa mwala? Kapena nsomba, nadzamninkha njoka m'malo mwa nsomba?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ndani wa inu ali atate, mwana wake akadzampempha mkate, adzampatsa mwala? Kapena nsomba, nadzamninkha njoka m'malo mwa nsomba?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndani mwa atatenu, mwana wake atampempha nsomba, iye nkumupatsa njoka?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Ndani mwa inu abambo, kodi mwana wanu atapempha nsomba, mʼmalo mwake mungamupatse njoka?

Onani mutuwo



Luka 11:11
5 Mawu Ofanana  

Kodi mkazi angaiwale mwana wake wa pabere, kuti iye sangachitire chifundo mwana wombala iye? Inde awa angaiwale, koma Ine sindingaiwale iwe.


Kapena pompempha nsomba, adzampatsa iye njoka kodi?


Kapena munthu ndani wa inu, amene pompempha mwana wake mkate, adzampatsa mwala?


Pakuti yense wakupempha alandira; ndi wofunayo apeza; ndi iye amene agogoda adzamtsegulira.


Kapena akadzampempha dzira kodi adzampatsa chinkhanira?