Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 1:62 - Buku Lopatulika

Ndipo anakodola atate wake, afuna amutche dzina liti?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anakodola atate wake, afuna amutche dzina liti?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono adalankhula ndi bambo wake ndi manja, namufunsa kuti, “Mukufuna kuti timutche dzina lanji?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo anapanga zizindikiro kwa abambo ake kuti adziwe dzina limene akanakonda kumutcha mwanayo.

Onani mutuwo



Luka 1:62
2 Mawu Ofanana  

Koma m'mene iye anatulukamo, sanathe kulankhula nao; ndipo anazindikira kuti iye adaona masomphenya mu Kachisimo. Ndipo iye analinkukodola iwo, nakhalabe wosalankhula.


Ndipo iwo anati kwa iye, Palibe wina wa abale ako amene atchedwa dzina ili.