Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 1:61 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo anati kwa iye, Palibe wina wa abale ako amene atchedwa dzina ili.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo anati kwa iye, Palibe wina wa abale ako amene atchedwa dzina ili.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo anthuwo adamuuza kuti, “Koma pakati pa abale anu palibe amene ali ndi dzina limeneli.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anati kwa iye, “Palibe mmodzi mwa abale ake amene ali ndi dzina limeneli.”

Onani mutuwo



Luka 1:61
3 Mawu Ofanana  

Ndipo amake anayankha, kuti, Iai; koma adzatchedwa Yohane.


Ndipo anakodola atate wake, afuna amutche dzina liti?


Kunali munthu, wotumidwa ndi Mulungu, dzina lake ndiye Yohane.