Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 1:60 - Buku Lopatulika

Ndipo amake anayankha, kuti, Iai; koma adzatchedwa Yohane.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo amake anayankha, kuti, Iai; koma adzatchedwa Yohane.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma mai wake adakana, adati, “Iyai, koma atchedwe Yohane.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

koma amayi ake anayankhula nati, “Ayi, atchulidwe kuti Yohane.”

Onani mutuwo



Luka 1:60
6 Mawu Ofanana  

natumiza ndi dzanja la Natani mneneriyo, namutcha dzina lake Wokondedwa ndi Yehova, chifukwa cha Yehova.


Ndipo ndinanka kwa mneneri wamkazi; ndipo iye anatenga pakati nabala mwana wamwamuna. Ndipo Yehova anati kwa ine, Utche dzina lake, Kangazakufunkha Fulumirakusakaza.


ndipo sanamdziwe iye kufikira atabala mwana wake; namutcha dzina lake Yesu.


Koma mngelo anati kwa iye, Usaope Zekariya, chifukwa kuti lamveka pemphero lako, ndipo mkazi wako Elizabeti adzakubalira mwana wamwamuna, ndipo udzamutcha dzina lake Yohane.


Ndipo iwo anati kwa iye, Palibe wina wa abale ako amene atchedwa dzina ili.


Ndipo iye anafunsa cholemberapo, nalemba, kuti, Dzina lake ndi Yohane. Ndipo anazizwa onse.