Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 1:56 - Buku Lopatulika

Ndipo Maria anakhala ndi iye ngati miyezi itatu, nabweranso kunyumba kwake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Maria anakhala ndi iye ngati miyezi itatu, nabweranso kunyumba kwake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Maria atakhala ndi Elizabeti ngati miyezi itatu, adabwerera kwao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mariya anakhala ndi Elizabeti pafupifupi miyezi itatu ndipo kenaka anabwerera kwawo.

Onani mutuwo



Luka 1:56
2 Mawu Ofanana  

(Monga analankhula kwa makolo athu) kwa Abrahamu ndi kwa mbeu yake kunthawi yonse.


Ndipo inakwanira nthawi ya Elizabeti, ya kubala kwake, ndipo anabala mwana wamwamuna.