Ndipo Maria anakhala ndi iye ngati miyezi itatu, nabweranso kunyumba kwake.
Maria atakhala ndi Elizabeti ngati miyezi itatu, adabwerera kwao.
Mariya anakhala ndi Elizabeti pafupifupi miyezi itatu ndipo kenaka anabwerera kwawo.
(Monga analankhula kwa makolo athu) kwa Abrahamu ndi kwa mbeu yake kunthawi yonse.
Ndipo inakwanira nthawi ya Elizabeti, ya kubala kwake, ndipo anabala mwana wamwamuna.