Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 1:47 - Buku Lopatulika

ndipo mzimu wanga wakondwera mwa Mulungu Mpulumutsi wanga,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo mzimu wanga wakondwera mwa Mulungu Mpulumutsi wanga,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndipo mzimu wanga ukukondwera mwa Mulungu, Mpulumutsi wanga,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo mzimu wanga ukondwera mwa Mulungu Mpulumutsi wanga,

Onani mutuwo



Luka 1:47
14 Mawu Ofanana  

Ndipo moyo wanga udzakondwera mwa Yehova; udzasekera mwa chipulumutso chake.


koma ndidzakondwera mwa Yehova, ndidzasekerera mwa Mulungu wa chipulumutso changa.


Kondwera kwambiri, mwana wamkazi wa Ziyoni; fuula mwana wamkazi wa Yerusalemu; taona, Mfumu yako ikudza kwa iwe; ndiye wolungama, ndi mwini chipulumutso; wofatsa ndi wokwera pabulu, ndi mwana wamphongo wa bulu.


pakuti wakubadwirani inu lero, m'mzinda wa Davide, Mpulumutsi, amene ali Khristu Ambuye.


Paulo, mtumwi wa Khristu Yesu monga mwa chilamuliro cha Mulungu Mpulumutsi wathu, ndi cha Khristu Yesu, chiyembekezo chathu:


Pakuti ichi nchokoma ndi cholandirika pamaso pa Mulungu Mpulumutsi wathu;


koma pa nyengo za Iye yekha anaonetsa mau ake muulalikiro, umene anandisungitsa ine, monga mwa lamulo la Mpulumutsi wathu Mulungu:


osatapa pa zao, komatu aonetsere chikhulupiriko chonse chabwino; kuti akakometsere chiphunzitso cha Mpulumutsi wathu Mulungu m'zinthu zonse.


akulindira chiyembekezo chodala, ndi maonekedwe a ulemerero wa Mulungu wamkulu ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu;


kwa Mulungu wayekha, Mpulumutsi wathu, mwa Yesu Khristu Ambuye wathu, kukhale ulemerero, ukulu, mphamvu, ndi ulamuliro zisanayambe nthawi, ndi tsopano, ndi kufikira nthawi zonse. Amen.