Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 1:40 - Buku Lopatulika

nalowa m'nyumba ya Zekariya, nalonjera Elizabeti.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

nalowa m'nyumba ya Zekariya, nalonjera Elizabeti.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adakaloŵa m'nyumba ya Zakariya, malonjera Elizabeti.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kumene anakalowa mʼnyumba ya Zakariya nalonjera Elizabeti.

Onani mutuwo



Luka 1:40
4 Mawu Ofanana  

Atate wako ndi amai ako akondwere, amai ako akukubala asekere.


Ndipo Maria ananyamuka masiku amenewa, namuka ndi changu kudziko la mapiri kumzinda wa Yuda;


Ndipo panali pamene Elizabeti anamva kulonjera kwake kwa Maria, mwana wosabadwayo anatsalima m'mimba mwake; ndipo Elizabeti anadzazidwa ndi Mzimu Woyera;


Masiku a Herode, mfumu ya Yudeya, kunali munthu wansembe, dzina lake Zakariya, wa gulu la ansembe la Abiya; ndi mkazi wake wa ana aakazi a fuko la Aroni, dzina lake Elizabeti.