Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 1:23 - Buku Lopatulika

Ndipo kunali, pamene masiku a utumiki wake anamalizidwa, anamuka kunyumba kwake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo kunali, pamene masiku a utumiki wake anamalizidwa, anamuka kunyumba kwake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Atatha masiku ake otumikira m'Nyumba ya Mulungu, adapita kwao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nthawi yake yotumikira itatha, anabwerera kwawo.

Onani mutuwo



Luka 1:23
4 Mawu Ofanana  

Ndi abale ao m'midzi mwao akafikafika, atapita masiku asanu ndi awiri masabata onse, kuti akhale nao;


Koma m'mene iye anatulukamo, sanathe kulankhula nao; ndipo anazindikira kuti iye adaona masomphenya mu Kachisimo. Ndipo iye analinkukodola iwo, nakhalabe wosalankhula.


Ndipo atatha masiku awa, Elizabeti mkazi wake anaima; nadzibisa miyezi isanu, nati,