Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 1:10 - Buku Lopatulika

Ndipo khamu lonse la anthu linalikupemphera kunja nthawi ya zonunkhira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo khamu lonse la anthu linalikupemphera kunja nthawi ya zonunkhira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Khamu lonse la anthu linkapemphera kunja pa nthaŵi yofukiza lubaniyo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo nthawi yofukiza lubani itafika, gulu lonse lopembedza linkapemphera kunja.

Onani mutuwo



Luka 1:10
7 Mawu Ofanana  

Pemphero langa liikike ngati chofukiza pamaso panu; kukweza manja anga kuikike ngati nsembe ya madzulo.


Ndipo anthu a m'dziko alambire pa chitseko cha chipata ichi pamaso pa Yehova pamasabata, ndi pokhala mwezi.


Ndipo musakhale munthu m'chihema chokomanako pakulowa iye kuchita chotetezera m'malo opatulika, kufikira atuluka, atachita chotetezera yekha, ndi mbumba yake, ndi msonkhano wonse wa Israele.


chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza;


Popeza tsono tili naye Mkulu wa ansembe wamkulu, wopyoza miyamba, Yesu mwana wa Mulungu, tigwiritsitse chivomerezo chathu.


Pakuti Khristu sanalowe m'malo opatulika omangika ndi manja, akutsanza oonawo; komatu mu Mwamba momwe, kuonekera tsopano pamaso pa Mulungu chifukwa cha ife;


Ndipo anadza mngelo wina, naima paguwa la nsembe, nakhala nacho chotengera cha zofukiza chagolide; ndipo anampatsa zofukiza zambiri, kuti aziike pamodzi ndi mapemphero a oyera mtima onse paguwa la nsembe lagolide, lokhala kumpando wachifumu.