Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Levitiko 7:3 - Buku Lopatulika

Ndipo achotseko, nabwere nao mafuta ake onse; mchira wamafuta, ndi mafuta akukuta matumbo,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo achotseko, nabwere nao mafuta ake onse; mchira wamafuta, ndi mafuta akukuta matumbo,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono apereke mafuta ake onse, mchira wamafuta ndi mafuta okuta matumbo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono apereke mafuta ake onse: mchira wamafuta ndi mafuta amene amakuta matumbo.

Onani mutuwo



Levitiko 7:3
9 Mawu Ofanana  

Nsembe za Mulungu ndizo mzimu wosweka; Inu, Mulungu, simudzaupeputsa mtima wosweka ndi wolapa.


Onani, Inu mukondwera ndi zoonadi m'malo a m'katimo; ndipo m'malo a m'tseri mudzandidziwitsa nzeru.


Musaidya yaiwisi, kapena yophika ndi madzi konse ai, koma yoocha pamoto; mutu wake ndi miyendo yake ndi matumbo ake.


Nutenge mafuta onse akukuta matumbo, ndi chokuta cha mphafa ndi impso ziwiri, ndi mafuta ali pa izo, ndi kuzitentha paguwa la nsembe.


Mwendo wathako wa ku dzanja lamanja ukhale gawo lake la iyeyu mwa ana a Aroni wakubwera nao mwazi wa zopereka zoyamika, ndi mafuta.