Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Levitiko 4:9 - Buku Lopatulika

ndi impso ziwiri ndi mafuta ali pomwepo, okhala m'chuuno, ndi chokuta cha mphafa chofikira kuimpso,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi impso ziwiri ndi mafuta ali pomwepo, okhala m'chuuno, ndi chokuta cha mphafa chofikira kuimpso,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Achotsenso imso ziŵiri pamodzi ndi mafuta ake omwe cham'chiwunomu, ndiponso mphumphu za mafuta akuchiŵindi ochotsa pamodzi ndi imso zija,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Achotsenso ndi kubwera ndi impsyo zonse ziwiri pamodzi ndi mafuta onse ndiponso mafuta onse amene aphimba chiwindi ndi impsyo

Onani mutuwo



Levitiko 4:9
3 Mawu Ofanana  

Nutenge mafuta onse akukuta matumbo, ndi chokuta cha mphafa ndi impso ziwiri, ndi mafuta ali pa izo, ndi kuzitentha paguwa la nsembe.


ndi impso ziwiri, ndi mafuta ali pomwepo okhala m'chuuno, ndi chokuta cha mphafa chofikira kuimpso.


umo azikachotsera pa ng'ombe ya nsembe yoyamika; ndipo wansembe azitenthe paguwa la nsembe yopsereza.