Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Levitiko 3:7 - Buku Lopatulika

akabwera nayo nkhosa kuti ikhale chopereka chake, abwere nayo pamaso pa Yehova;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

akabwera nayo nkhosa kuti ikhale chopereka chake, abwere nayo pamaso pa Yehova;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akapereka nkhosa kuti ikhale nsembe, abwere nayo pamaso pa Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati apereka nsembe ya mwana wankhosa, abwere naye pamaso pa Yehova.

Onani mutuwo



Levitiko 3:7
9 Mawu Ofanana  

Ndipo mfumu ndi anthu onse a Israele pamodzi naye anaphera nsembe pamaso pa Yehova.


Ndipo chopereka chake chikakhala nsembe yoyamika; akabwera nayo ng'ombe, kapena yaimuna kapena yaikazi, azibwera nayo yopanda chilema pamaso pa Yehova.


pamenepo iye wobwera nacho chopereka chake kwa Yehova, azibwera nayo nsembe yaufa, limodzi la magawo khumi la efa wa ufa wosalala, wosakaniza ndi limodzi la magawo anai la hini la mafuta;


ndipo uzikonzera nsembe yopsereza kapena yophera, vinyo wa nsembe yothira, limodzi la magawo anai la hini, ukhale wa mwanawankhosa mmodzi.


Mwanawankhosa mmodziyo umpereke m'mawa, ndi mwanawankhosa winayo umpereke madzulo;


pakuti zochitidwa nao m'tseri, kungakhale kuzinena kuchititsa manyazi.


ndipo yendani m'chikondi monganso Khristu anakukondani inu, nadzipereka yekha m'malo mwathu, chopereka ndi nsembe kwa Mulungu, ikhale fungo lonunkhira bwino.


koposa kotani nanga mwazi wa Khristu amene anadzipereka yekha wopanda chilema kwa Mulungu mwa Mzimu wosatha, udzayeretsa chikumbumtima chanu kuchisiyanitsa ndi ntchito zakufa, kukatumikira Mulungu wamoyo?