Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Levitiko 2:6 - Buku Lopatulika

Uphwanye, nuthirepo mafuta; ndiyo nsembe yaufa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Uphwanye, nuthirepo mafuta; ndiyo nsembe yaufa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Umuduledule ndi kumupaka mafuta. Chimenecho ndicho chopereka cha chakudya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Umuduledule bulediyo ndi kumupaka mafuta; imeneyo ndi nsembe yachakudya.

Onani mutuwo



Levitiko 2:6
6 Mawu Ofanana  

Ndipo asende nsembe yopsereza, ndi kuikadzula ziwalo zake.


Ndipo nsembe yaufa yako ikakhala yokazinga m'chiwaya, ikhale ya ufa wosalala wopanda chotupitsa, wosakaniza ndi mafuta.


Ndipo chopereka chako chikakhala nsembe yaufa ya mumphika, chikhale cha ufa wosalala ndi mafuta.