Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Levitiko 11:3 - Buku Lopatulika

Nyama iliyonse yogawanika chiboda, nikhala yogawanikadi chiboda, ndi yobzikula, imeneyo muyenera kudya.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nyama iliyonse yogawanika chiboda, nikhala yogawanikadi chiboda, ndi yobzikula, imeneyo muyenera kudya.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

‘Nyama zonse zokhala ndi ziboda zogaŵikana, ndi zobzikula, angathe kudya zimenezo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nyama iliyonse imene ili ndi chipondero chogawikana pakati ndi yobzikula mukhoza kudya.

Onani mutuwo



Levitiko 11:3
17 Mawu Ofanana  

Pakuti nzeru idzalowa m'mtima mwako, moyo wako udzakondwera ndi kudziwa,


Lekani, achibwana inu, nimukhale ndi moyo; nimuyende m'njira ya nzeru.


Nenani ndi ana a Israele, ndi kuti, Izi ndi zamoyo zimene muyenera kumadya mwa nyama zonse zili padziko lapansi.


Nyama iliyonse yakugawanika chiboda, koma yosagawanikitsa, ndi yosabzikula, muiyese yodetsa; aliyense wakuikhudza adzakhala wodetsedwa.


Koma izi zokha simuyenera kuzidya mwa zobzikulazo, kapena zogawanika chiboda; ngamira, ingakhale ibzikula, koma yosagawanika chiboda, muziiyesa yodetsedwa.


Ndi mbira, ingakhale ibzikula koma yosagawanika chiboda, muiyese yodetsedwa.


Ndi kalulu, popeza abzikula koma wosagawanika chiboda, mumuyese wodetsedwa.


Ndi nkhumba, popeza igawanika chiboda, nikhala yogawanikadi chiboda, koma yosabzikula, muiyese yodetsedwa.


Amenewa anali mfulu koposa a mu Tesalonika, popeza analandira mau ndi kufunitsa kwa mtima wonse, nasanthula m'malembo masiku onse, ngati zinthu zinali zotero.


Chifukwa chake, Tulukani pakati pao, ndipo patukani, ati Ambuye, Ndipo musakhudza kanthu kosakonzeka; ndipo Ine ndidzalandira inu,


Ndipo nyama iliyonse yogawanika chiboda, nikhala yogawanikadi chiboda, nibzikula, imeneyo muyenera kudya.


ndi nkhumba, popeza igawanika chiboda koma yosabzikula, muiyese yodetsa; musamadya nyama yao, musamakhudza mitembo yao.


Izi uzisamalitse; mu izi ukhale; kuti kukula mtima kwako kuonekere kwa onse.