Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Levitiko 1:6 - Buku Lopatulika

Ndipo asende nsembe yopsereza, ndi kuikadzula ziwalo zake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo asende nsembe yopsereza, ndi kuikadzula ziwalo zake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo asende nyamayo ndi kuidula nthulinthuli.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Munthuyo asende nsembe yopserezayo ndi kuyidula nthulinthuli.

Onani mutuwo



Levitiko 1:6
6 Mawu Ofanana  

Yehova Mulungu ndipo anapangira Adamu ndi mkazi wake malaya azikopa, nawaveka iwo.


Ndipo anakonza nkhunizo, naduladula ng'ombe, naiika pankhuni. Nati, Dzazani madzi mbiya zinai, muwathire pa nsembe yopsereza ndi pankhuni.


Ndi zichiri zangowe, chikhato m'litali mwake, zinamangika m'katimo pozungulirapo; ndi pamagome panali nyama ya nsembe.


Ndipo ana a Aroni wansembeyo asonkhe moto paguwa la nsembe, ndi kukonza nkhuni pamotopo;


Uphwanye, nuthirepo mafuta; ndiyo nsembe yaufa.


Ndipo chikopa cha nsembe yopsereza chikhale chakechake cha wansembe, amene anabwera nayo nsembe yopsereza ya munthu aliyense.