Hoseya 3:5 - Buku Lopatulika
atatero ana a Israele adzabwera, nadzafuna Yehova Mulungu wao, ndi Davide mfumu yao, nadzafika ndi mantha kwa Yehova, ndi ku ukoma wake masiku otsiriza.
Onani mutuwo
atatero ana a Israele adzabwera, nadzafuna Yehova Mulungu wao, ndi Davide mfumu yao, nadzafika ndi mantha kwa Yehova, ndi ku ukoma wake masiku otsiriza.
Onani mutuwo
Pambuyo pake Aisraelewo adzabwerera ndi kufunafuna Chauta Mulungu wao ndi mdzukulu wa Davide mfumu yao. Nthaŵi imeneyo Aisraele adzagonja kwa Chauta ndipo adzalandira zabwino zake.
Onani mutuwo
Pambuyo pake Aisraeli adzabwerera ndi kufunafuna Yehova Mulungu wawo ndi Davide mfumu yawo. Adzabwera kwa Yehova akunjenjemera ndipo adzalandira madalitso mʼmasiku awo otsiriza.
Onani mutuwo