Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 7:24 - Buku Lopatulika

Ndipo anapambana madzi padziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Madziwo adakhala osaphwa konse pa dziko lapansi masiku 150.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Madziwo anadzaza dziko lonse lapansi kwa masiku 150.

Onani mutuwo



Genesis 7:24
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Mulungu anakumbukira Nowa ndi zamoyo zonse, ndi nyama zonse zimene zinali pamodzi naye m'chingalawamo; ndipo Mulungu anapititsa mphepo padziko lapansi, naphwa madzi;