Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 6:21 - Buku Lopatulika

Ndipo iwe udzitengereko wekha zakudya zonse zodyedwa, nudzisonkhanitsire izi wekha: ndipo zidzakhala zakudya za iwe ndi za iwo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwe udzitengereko wekha zakudya zonse zodyedwa, nudzisonkhanitsire izi wekha: ndipo zidzakhala zakudya za iwe ndi za iwo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Udzatengenso zakudya za mtundu uliwonse kuti inu ndi nyamazo muzidzadya.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Udzatengenso chakudya cha mtundu uliwonse ndi kuchisunga kuti inu ndi nyamazo muzidzadya.”

Onani mutuwo



Genesis 6:21
9 Mawu Ofanana  

Amkonzeratu khwangwala chakudya chake ndani, pamenepo ana ake afuulira kwa Mulungu, naulukauluka osowa chakudya?


Pakuti mapiri aiphukitsira chakudya, kumene zisewera nyama zonse zakuthengo.


Ndiye wakupatsa nyama zonse chakudya; pakuti chifundo chake nchosatha.


Muolowetsa dzanja lanu, nimukwaniritsira zamoyo zonse chokhumba chao.


Amene apatsa zoweta chakudya chao, ana a khwangwala alikulira.


Njira yao ikhale ya mdima ndi yoterera, ndipo mngelo wa Yehova awalondole.


Yang'anirani mbalame za kumwamba, kuti sizimafesa ai, kapena sizimatema ai, kapena sizimatutira m'nkhokwe; ndipo Atate wanu wa Kumwamba azidyetsa. Nanga inu mulibe kusiyana nazo kuziposa kodi?