Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 50:6 - Buku Lopatulika

Ndipo Farao anati, Pita, kaike atate wako, monga iye anakulumbiritsa iwe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Farao anati, Pita, kaike atate wako, monga iye anakulumbiritsa iwe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Farao adamuyankha kuti, “Pita ukaike atate ako monga momwe adakulumbiritsira.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Farao anati, “Pita ukayike abambo ako monga anakulumbiritsa kuti uchite.”

Onani mutuwo



Genesis 50:6
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Israele anati kwa Yosefe, Taona, ndilinkufa ine; Mulungu adzakhala ndi iwe, adzakubwezanso iwe ku dziko la makolo ako.


Atate wanga anandilumbiritsa ine, kuti, Taona, ndilinkufa; m'manda m'mene ndadzikonzeratu ndekha m'dziko la Kanani, m'menemo udzandiika ine. Tsopano mundiloletu, ndikwereko, ndipite, ndikaike atate wanga, nditatero ndidzabweranso.


Ndipo Yosefe anapita kukaika atate wake; ndipo anakwera pamodzi ndi akapolo onse a Farao, ndi akulu a pa mbumba yake, ndi akulu onse a m'dziko la Ejipito,