Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 50:16 - Buku Lopatulika

Ndipo anatumiza mthenga kwa Yosefe kuti, Atate wathu asanafe analamulira, kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anatumiza mthenga kwa Yosefe kuti, Atate wathu asanafe analamulira, kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero adatumiza mau kwa Yosefe kuti, “Atate anu asanafe adanena mau akuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Motero anatumiza mawu kwa Yosefe kuti, “Abambo anu anasiya malangizo asanafe nati:

Onani mutuwo



Genesis 50:16
3 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene abale ake a Yosefe anaona kuti atate wao anafa, anati, Kapena Yosefe adzatida ife, ndipo adzatibwezera ife zoipa zonse tidamchitira iye.


Muziti chotero kwa Yosefe, Mukhululukiretu tsopano kulakwa kwa abale anu, ndi kuchimwa kwao, chifukwa kuti anakuchitirani inu choipa; tsopano mutikhululukiretu kulakwa kwa akapolo a Mulungu wa atate wanu. Ndipo Yosefe analira pamene iwo ananena ndi iye.


Kuopa anthu kutchera msampha; koma wokhulupirira Yehova adzapulumuka.