Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 5:31 - Buku Lopatulika

masiku ake onse a Lameki anali zaka mazana asanu ndi awiri kudza makumi asanu ndi awiri; ndipo anamwalira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

masiku ake onse a Lameki anali zaka mazana asanu ndi awiri kudza makumi asanu ndi awiri; ndipo anamwalira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adamwalira ali wa zaka 777.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zaka zonse za Lameki zinali 777, ndipo kenaka anamwalira.

Onani mutuwo



Genesis 5:31
2 Mawu Ofanana  

ndipo Lameki anakhala ndi moyo atabala Nowa, zaka mazana asanu kudza makumi asanu ndi anai ndi zisanu, nabala ana aamuna ndi aakazi:


Ndipo Nowa anali wa zaka mazana asanu; ndipo Nowa anabala Semu ndi Hamu ndi Yafeti.