Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 5:28 - Buku Lopatulika

Ndipo Lameki anakhala ndi moyo zaka zana kudza makumi asanu ndi atatu ndi ziwiri, nabala mwana wamwamuna;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Lameki anakhala ndi moyo zaka zana kudza makumi asanu ndi atatu ndi ziwiri, nabala mwana wamwamuna;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Lameki ali wa zaka 182, adabereka mwana,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Lameki anali ndi zaka 182, anabereka mwana wamwamuna.

Onani mutuwo



Genesis 5:28
3 Mawu Ofanana  

masiku ake onse a Metusela anali mazana asanu ndi anai kudza makumi asanu ndi limodzi kudza zisanu ndi zinai; ndipo anamwalira.


namutcha dzina lake Nowa, ndi kuti, Yemweyu adzatonthoza mtima wathu pantchito zathu zovuta za manja athu, chifukwa cha nthaka imene anaitemberera Yehova;


mwana wa Kainani, mwana wa Arifaksadi, mwana wa Semu, mwana wa Nowa, mwana wa Lameki,