Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 5:25 - Buku Lopatulika

Ndipo Metusela anakhala ndi moyo zaka zana kudza makumi asanu ndi atatu ndi zisanu ndi ziwiri, nabala Lameki;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Metusela anakhala ndi moyo zaka zana kudza makumi asanu ndi atatu ndi zisanu ndi ziwiri, nabala Lameki;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Metusela ali wa zaka 187, adabereka mwana dzina lake Lameki,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Metusela anali ndi zaka 187, anabereka Lameki.

Onani mutuwo



Genesis 5:25
3 Mawu Ofanana  

Kwa Enoki ndipo kunabadwa Iradi; Iradi ndipo anabala Mehuyaele; Mehuyaele ndipo anabala Metusaele; Metusaele ndipo anabala Lameki.


ndipo Enoki anayendabe ndi Mulungu; ndipo panalibe iye; pakuti Mulungu anamtenga.


ndipo Metusela anakhala ndi moyo, atabala Lameki, zaka mazana asanu ndi awiri kudza makumi asanu ndi atatu ndi ziwiri, nabala ana aamuna ndi aakazi: