Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 5:20 - Buku Lopatulika

masiku ake onse a Yaredi anali zaka mazana asanu ndi anai kudza makumi asanu ndi limodzi ndi ziwiri: ndipo anamwalira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

masiku ake onse a Yaredi anali zaka mazana asanu ndi anai kudza makumi asanu ndi limodzi ndi ziwiri: ndipo anamwalira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adamwalira ali wa zaka 962.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zaka zonse za Yaredi zinali 962 ndipo anamwalira.

Onani mutuwo



Genesis 5:20
3 Mawu Ofanana  

ndipo Yaredi anakhala ndi moyo, atabala Enoki, zaka mazana asanu ndi atatu, nabala ana aamuna ndi aakazi;


Ndipo Enoki anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi limodzi kudza zisanu, nabala Metusela:


Ndipo masiku onse a Nowa anali mazana asanu ndi anai kudza makumi asanu: ndipo anamwalira.