Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 5:15 - Buku Lopatulika

Ndipo Mahalalele anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi limodzi kudza zisanu, nabala Yaredi;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mahalalele anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi limodzi kudza zisanu, nabala Yaredi;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mahalalele ali wa zaka 65 adabereka Yaredi,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Mahalaleli anali ndi zaka 65, anabereka Yaredi.

Onani mutuwo



Genesis 5:15
5 Mawu Ofanana  

masiku ake onse a Kenani anali zaka mazana asanu ndi anai kudza khumi; ndipo anamwalira.


ndipo Mahalalele anakhala ndi moyo, atabala Yaredi, zaka mazana asanu ndi atatu kudza makumi atatu, nabala ana aamuna ndi aakazi:


Ndipo Enoki anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi limodzi kudza zisanu, nabala Metusela:


Kenani, Mahalalele, Yaredi,


mwana wa Metusela, mwana wa Enoki, mwana wa Yaredi, mwana wa Mahalalele, mwana wa Kainani,