Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 49:5 - Buku Lopatulika

Simeoni ndi Levi ndiwo abale; zida za mphulupulu ndizo malupanga ao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Simeoni ndi Levi ndiwo abale; zida za mphulupulu ndizo malupanga ao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Simeoni ndi Levi mpachibale pao, amagwiritsa ntchito zida zankhondo pochita chiwawa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Simeoni ndi Levi ndi pachibale pawo, anachitira nkhanza anthu amene anachita nawo pangano.

Onani mutuwo



Genesis 49:5
8 Mawu Ofanana  

Wogwira ntchito mwaulesi ndiye mbale wake wa wosakaza.


Ndi kumalire a Benjamini, kuyambira mbali ya kum'mawa kufikira mbali ya kumadzulo; Simeoni, gawo limodzi.


Wa fuko la ana a Simeoni, Semuele mwana wa Amihudi.


Motero ana a Israele anapatsa Alevi mizinda iyi ndi mabusa ao, molota maere, monga Yehova adalamulira mwa dzanja la Mose.


Mwa fuko la Simeoni zikwi khumi ndi ziwiri. Mwa fuko Levi zikwi khumi ndi ziwiri. Mwa fuko la Isakara zikwi khumi ndi ziwiri.