Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 49:32 - Buku Lopatulika

munda ndi phanga lili m'menemo, zinagulidwa kwa ana a Hiti

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

munda ndi phanga lili m'menemo, zinagulidwa kwa ana a Hiti

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mundawo pamodzi ndi phangalo adagula kwa Ahiti.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Munda ndi manda amene ali mʼmenemo zinagulidwa kwa Ahiti.”

Onani mutuwo



Genesis 49:32
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Kanani anabala Sidoni woyamba wake, ndi Heti,


pamenepo anaika Abrahamu ndi Sara mkazi wake; pamenepo anaika Isaki ndi Rebeka mkazi wake: pamenepo ndinaika Leya:


Pamene Yakobo anatha kulangiza ana ake aamuna, anafunya mapazi ake pakama, natsirizika, nasonkhanitsidwa kwa anthu a mtundu wake.